×

Ndipo onse osakhulupirira adzatengedwa paulendo wa ku Gahena m’magulumagulu ndipo pamene azidzafika 39:71 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zumar ⮕ (39:71) ayat 71 in Chichewa

39:71 Surah Az-Zumar ayat 71 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zumar ayat 71 - الزُّمَر - Page - Juz 24

﴿وَسِيقَ ٱلَّذِينَ كَفَرُوٓاْ إِلَىٰ جَهَنَّمَ زُمَرًاۖ حَتَّىٰٓ إِذَا جَآءُوهَا فُتِحَتۡ أَبۡوَٰبُهَا وَقَالَ لَهُمۡ خَزَنَتُهَآ أَلَمۡ يَأۡتِكُمۡ رُسُلٞ مِّنكُمۡ يَتۡلُونَ عَلَيۡكُمۡ ءَايَٰتِ رَبِّكُمۡ وَيُنذِرُونَكُمۡ لِقَآءَ يَوۡمِكُمۡ هَٰذَاۚ قَالُواْ بَلَىٰ وَلَٰكِنۡ حَقَّتۡ كَلِمَةُ ٱلۡعَذَابِ عَلَى ٱلۡكَٰفِرِينَ ﴾
[الزُّمَر: 71]

Ndipo onse osakhulupirira adzatengedwa paulendo wa ku Gahena m’magulumagulu ndipo pamene azidzafika pafupi, makomo ake adzatsekulidwa ndipo oyang’anira kumeneko adzati kwa iwo, “Kodi sikunadze kwa inu Atumwi a mtundu wanu kukulalikirani ulangizi wa Ambuye wanu ndi kukuchenjezani za kukumana kwanu ndi tsiku lino?” Iwo adzati, “Inde!” Koma chilango chakwaniritsidwa kwa anthu osakhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وسيق الذين كفروا إلى جهنم زمرا حتى إذا جاءوها فتحت أبوابها وقال, باللغة نيانجا

﴿وسيق الذين كفروا إلى جهنم زمرا حتى إذا جاءوها فتحت أبوابها وقال﴾ [الزُّمَر: 71]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene adakanira, adzakusidwa kunka ku Jahannam ali magulumagulu kufikira pomwe adzaifikira, makomo ake adzatsekulidwa, ndipo alonda ake adzawauza: “Kodi sadakudzereni aneneri ochokera mwa inu okulakatulirani zisonyezo za Mbuye wanu, ndi kukuchenjezani za kukumana kwanu ndi tsiku lanuli?” Adzayankha (nati): “Inde, adatidzera; koma lidatsimikizika liwu la chilango pa okanira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek