×

oh inu anthu okhulupirira! Khalani anthu ochita chilungamo ngati mboni za Mulungu 4:135 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:135) ayat 135 in Chichewa

4:135 Surah An-Nisa’ ayat 135 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 135 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿۞ يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ كُونُواْ قَوَّٰمِينَ بِٱلۡقِسۡطِ شُهَدَآءَ لِلَّهِ وَلَوۡ عَلَىٰٓ أَنفُسِكُمۡ أَوِ ٱلۡوَٰلِدَيۡنِ وَٱلۡأَقۡرَبِينَۚ إِن يَكُنۡ غَنِيًّا أَوۡ فَقِيرٗا فَٱللَّهُ أَوۡلَىٰ بِهِمَاۖ فَلَا تَتَّبِعُواْ ٱلۡهَوَىٰٓ أَن تَعۡدِلُواْۚ وَإِن تَلۡوُۥٓاْ أَوۡ تُعۡرِضُواْ فَإِنَّ ٱللَّهَ كَانَ بِمَا تَعۡمَلُونَ خَبِيرٗا ﴾
[النِّسَاء: 135]

oh inu anthu okhulupirira! Khalani anthu ochita chilungamo ngati mboni za Mulungu ngakhale kuti umboniwo ndi wosakomera inu kapena makolo anu kapena abale anu, kaya iwo ndi wolemera kapena wosauka. Mulungu ndiye Mtetezi wa iwo onse. Motero musatsatire zilakolako zanu ndi kusiya kuchita chilungamo. Ndipo ngati mukapereka umboni wosayenera kapena kukana kupereka, ndithudi Mulungu ali kudziwa ntchito zanu zimene muchita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا كونوا قوامين بالقسط شهداء لله ولو على أنفسكم أو, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا كونوا قوامين بالقسط شهداء لله ولو على أنفسكم أو﴾ [النِّسَاء: 135]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Khalani oimiritsa chilungamo, opereka umboni chifukwa cha Allah; ngakhale kuti ubwere ndi masautso kwa inu, kapena kwa makolo anu, kapena kwa abale anu, ngakhale ali olemera kapena osauka, (musayang’ane zimenezo). Allah ndiye woyenera kuyang’ana za awiriwo. Choncho musatsate zilakolako ndi kusiya chilungamo. Ngati mukhotetsa (umboni), kapena kupewa (kupereka umboni) ndithudi nkhani zonse zomwe mukuchita Allah akuzidziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek