×

Koma iwo ozindikira kwambiri amene ali pakati pawo ndi okhulupirira amene amakhulupirira 4:162 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:162) ayat 162 in Chichewa

4:162 Surah An-Nisa’ ayat 162 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 162 - النِّسَاء - Page - Juz 6

﴿لَّٰكِنِ ٱلرَّٰسِخُونَ فِي ٱلۡعِلۡمِ مِنۡهُمۡ وَٱلۡمُؤۡمِنُونَ يُؤۡمِنُونَ بِمَآ أُنزِلَ إِلَيۡكَ وَمَآ أُنزِلَ مِن قَبۡلِكَۚ وَٱلۡمُقِيمِينَ ٱلصَّلَوٰةَۚ وَٱلۡمُؤۡتُونَ ٱلزَّكَوٰةَ وَٱلۡمُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِ أُوْلَٰٓئِكَ سَنُؤۡتِيهِمۡ أَجۡرًا عَظِيمًا ﴾
[النِّسَاء: 162]

Koma iwo ozindikira kwambiri amene ali pakati pawo ndi okhulupirira amene amakhulupirira mu zimene zavumbulutsidwa kwa iwe ndi zimene zidavumbulitsidwa iwe usanadze, ndipo amapemphera nthawi zonse ndikupereka msonkho wothandiza anthu osauka ndipo ali ndi chikhulupiriro mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza, awa ndiwo amene Ife tidzawapatsa mphotho yaikulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لكن الراسخون في العلم منهم والمؤمنون يؤمنون بما أنـزل إليك وما أنـزل, باللغة نيانجا

﴿لكن الراسخون في العلم منهم والمؤمنون يؤمنون بما أنـزل إليك وما أنـزل﴾ [النِّسَاء: 162]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma mwa iwo amene azama pa maphunziro, ndi okhulupirira (onsewo) akukhulupirira zimene zavumbulutsidwa kwa iwe ndi zimene zidavumbulutsidwa patsogolo pako. Ndipo omwe akupitiriza kupemphera Swala, ndi kupereka Zakaati, ndi kukhulupirira Allah komanso tsiku lachimaliziro, iwo tidzawapatsa malipiro aakulu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek