×

Koma Mulungu achitira umboni pa zimene wavumbulutsakwaiwe, Iyewalitumizandinzeruzakendipo angelo achitira umboni. Ndipo 4:166 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:166) ayat 166 in Chichewa

4:166 Surah An-Nisa’ ayat 166 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 166 - النِّسَاء - Page - Juz 6

﴿لَّٰكِنِ ٱللَّهُ يَشۡهَدُ بِمَآ أَنزَلَ إِلَيۡكَۖ أَنزَلَهُۥ بِعِلۡمِهِۦۖ وَٱلۡمَلَٰٓئِكَةُ يَشۡهَدُونَۚ وَكَفَىٰ بِٱللَّهِ شَهِيدًا ﴾
[النِّسَاء: 166]

Koma Mulungu achitira umboni pa zimene wavumbulutsakwaiwe, Iyewalitumizandinzeruzakendipo angelo achitira umboni. Ndipo Mulungu ndi wokwana kukhalamboni

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لكن الله يشهد بما أنـزل إليك أنـزله بعلمه والملائكة يشهدون وكفى بالله, باللغة نيانجا

﴿لكن الله يشهد بما أنـزل إليك أنـزله بعلمه والملائكة يشهدون وكفى بالله﴾ [النِّسَاء: 166]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma Allah akuikira umboni zimene wakuvumbulutsira kuti (nzoona), adavumbulutsa mwanzeru Zake. Nawonso angelo akuikira umboni. Ndipo Allah akukwana kukhala mboni
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek