×

Kodi mwatani kuti mukhale ogawikana magulu awiri pa nkhani ya anthu a 4:88 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:88) ayat 88 in Chichewa

4:88 Surah An-Nisa’ ayat 88 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 88 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿۞ فَمَا لَكُمۡ فِي ٱلۡمُنَٰفِقِينَ فِئَتَيۡنِ وَٱللَّهُ أَرۡكَسَهُم بِمَا كَسَبُوٓاْۚ أَتُرِيدُونَ أَن تَهۡدُواْ مَنۡ أَضَلَّ ٱللَّهُۖ وَمَن يُضۡلِلِ ٱللَّهُ فَلَن تَجِدَ لَهُۥ سَبِيلٗا ﴾
[النِّسَاء: 88]

Kodi mwatani kuti mukhale ogawikana magulu awiri pa nkhani ya anthu a chinyengo? Mulungu, mwini wake wawataya chifukwa cha ntchito zawo zoipa. Kodi inu mufuna kumutsogolera iye amene Mulungu wamusokeretsa? Inu simudzapeza njira ina iliyonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فما لكم في المنافقين فئتين والله أركسهم بما كسبوا أتريدون أن تهدوا, باللغة نيانجا

﴿فما لكم في المنافقين فئتين والله أركسهم بما كسبوا أتريدون أن تهدوا﴾ [النِّسَاء: 88]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi mwatani inu pokhala magulu awiri pa nkhani ya achiphamaso (achinyengo) pomwe Allah wawatembenuza chifukwa cha (zoipa) zomwe achita? Kodi mukufuna kuti mumuongole amene Allah wamlekelera kusokera? Ndipo amene Allah wamulekelera kusokera, simungathe kumpezera njira (yomuikira ku chilungamo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek