×

Iwo afuna kuti iwe usakhulupirire monga momwe iwo sadakhulupirire kuti mulingane. Iwe 4:89 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:89) ayat 89 in Chichewa

4:89 Surah An-Nisa’ ayat 89 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 89 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿وَدُّواْ لَوۡ تَكۡفُرُونَ كَمَا كَفَرُواْ فَتَكُونُونَ سَوَآءٗۖ فَلَا تَتَّخِذُواْ مِنۡهُمۡ أَوۡلِيَآءَ حَتَّىٰ يُهَاجِرُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِۚ فَإِن تَوَلَّوۡاْ فَخُذُوهُمۡ وَٱقۡتُلُوهُمۡ حَيۡثُ وَجَدتُّمُوهُمۡۖ وَلَا تَتَّخِذُواْ مِنۡهُمۡ وَلِيّٗا وَلَا نَصِيرًا ﴾
[النِّسَاء: 89]

Iwo afuna kuti iwe usakhulupirire monga momwe iwo sadakhulupirire kuti mulingane. Iwe usapalane nawo ubwenzi ayi mpaka pamene asiya nyumba zawo chifukwa cha njira ya Mulungu. Koma ngati iwo akuthawani, agwireni ndipo muwaphe pali ponse pamene muwapeze ndipo musafune abwenzi kapena okuthandizani pakati pawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ودوا لو تكفرون كما كفروا فتكونون سواء فلا تتخذوا منهم أولياء حتى, باللغة نيانجا

﴿ودوا لو تكفرون كما كفروا فتكونون سواء فلا تتخذوا منهم أولياء حتى﴾ [النِّسَاء: 89]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akufuna kuti mukadakhala osakhulupirira monga momwe iwo sadakhulupirire tero kuti mukhale ofanana. Musawachite kukhala abwenzi mpaka asamukire panjira ya Allah. Koma ngati anyoza, agwireni ndi kuwapha paliponse mwawapeza (monga momwe akukuchitirani inu). Ndipo musamuyese mtetezi ngakhale mthandizi aliyense wa iwo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek