×

Mudzawapeza ena ali kufuna chitetezo chanu ndiponso chitetezo chochokera kwa anthu awo. 4:91 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah An-Nisa’ ⮕ (4:91) ayat 91 in Chichewa

4:91 Surah An-Nisa’ ayat 91 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah An-Nisa’ ayat 91 - النِّسَاء - Page - Juz 5

﴿سَتَجِدُونَ ءَاخَرِينَ يُرِيدُونَ أَن يَأۡمَنُوكُمۡ وَيَأۡمَنُواْ قَوۡمَهُمۡ كُلَّ مَا رُدُّوٓاْ إِلَى ٱلۡفِتۡنَةِ أُرۡكِسُواْ فِيهَاۚ فَإِن لَّمۡ يَعۡتَزِلُوكُمۡ وَيُلۡقُوٓاْ إِلَيۡكُمُ ٱلسَّلَمَ وَيَكُفُّوٓاْ أَيۡدِيَهُمۡ فَخُذُوهُمۡ وَٱقۡتُلُوهُمۡ حَيۡثُ ثَقِفۡتُمُوهُمۡۚ وَأُوْلَٰٓئِكُمۡ جَعَلۡنَا لَكُمۡ عَلَيۡهِمۡ سُلۡطَٰنٗا مُّبِينٗا ﴾
[النِّسَاء: 91]

Mudzawapeza ena ali kufuna chitetezo chanu ndiponso chitetezo chochokera kwa anthu awo. Nthawi iliyonse akayesedwa iwo amapita mwamsangamsanga. Ngati iwo sachoka kwa inu ndiponso ngati iwo sakhazikitsa mtendere ndi inu kapena kusiya nkhondo ndi inu, agwireni ndi kuwapha pali ponse pamene muwapeza. Pa anthu otere, Ife takupatsani chilolezo chomenyana nawo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ستجدون آخرين يريدون أن يأمنوكم ويأمنوا قومهم كل ما ردوا إلى الفتنة, باللغة نيانجا

﴿ستجدون آخرين يريدون أن يأمنوكم ويأمنوا قومهم كل ما ردوا إلى الفتنة﴾ [النِّسَاء: 91]

Khaled Ibrahim Betala
“Muzawapeza ena omwe akufuna kupeza chitetezo kwa inu ndi kupeza chitetezo kwa anthu awo. Nthawi iliyonse akabwezedwa ku ukafiri (ndi anzawo osakhulupirira), amagweramo mwamtheradi (nkuyamba kumenyananso ndi inu), ngati sadzipatula kwa inu ndipo osakupatsani mtendere ndi kutsekereza manja awo, agwireni ndi kuwapha paliponse pamene mwawapeza (monga momwe iwo akuchitira kwa inu) ndipo takupangirani chisonyezo choonekera pa iwo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek