×

Ndithudi Ife tidatumiza Atumwi iwe usanabadwe. Alipo ena amene takuuza za iwo 40:78 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ghafir ⮕ (40:78) ayat 78 in Chichewa

40:78 Surah Ghafir ayat 78 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ghafir ayat 78 - غَافِر - Page - Juz 24

﴿وَلَقَدۡ أَرۡسَلۡنَا رُسُلٗا مِّن قَبۡلِكَ مِنۡهُم مَّن قَصَصۡنَا عَلَيۡكَ وَمِنۡهُم مَّن لَّمۡ نَقۡصُصۡ عَلَيۡكَۗ وَمَا كَانَ لِرَسُولٍ أَن يَأۡتِيَ بِـَٔايَةٍ إِلَّا بِإِذۡنِ ٱللَّهِۚ فَإِذَا جَآءَ أَمۡرُ ٱللَّهِ قُضِيَ بِٱلۡحَقِّ وَخَسِرَ هُنَالِكَ ٱلۡمُبۡطِلُونَ ﴾
[غَافِر: 78]

Ndithudi Ife tidatumiza Atumwi iwe usanabadwe. Alipo ena amene takuuza za iwo ndipo alipo ena amene sitidakuuze za iwo ndipo sichidali choyenera kuti Mtumwi abweretse chizindikiro kupatula ndi chilolezo cha Mulungu. Koma pamene ulamuliro wa Mulungu udadza, chiweruzo chidaperekedwa mwachilungamo. Ndipo onse, amene ankati ndi zabodza, adatayika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد أرسلنا رسلا من قبلك منهم من قصصنا عليك ومنهم من لم, باللغة نيانجا

﴿ولقد أرسلنا رسلا من قبلك منهم من قصصنا عليك ومنهم من لم﴾ [غَافِر: 78]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithu tidawatuma atumiki patsogolo pako; ena mwa iwo tidakusimbira (nkhani zawo ndi maina awo). Ena mwa iwo sitidakusimbire. Sikudali kotheka kwa mtumiki aliyense kudzetsa chozizwitsa mwa yekha, koma ndi chifuniro cha Allah. Ndipo lamulo la Allah likadzadza, kudzaweruzidwa mwa choonadi. Ndipo ochita zachabe panthawi imeneyo adzataika; (adzaluza)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek