×

okhawo amene sakhulupilira amafuna kuti ola lidze msanga pamene onse amene amakhulupirira 42:18 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:18) ayat 18 in Chichewa

42:18 Surah Ash-Shura ayat 18 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 18 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿يَسۡتَعۡجِلُ بِهَا ٱلَّذِينَ لَا يُؤۡمِنُونَ بِهَاۖ وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مُشۡفِقُونَ مِنۡهَا وَيَعۡلَمُونَ أَنَّهَا ٱلۡحَقُّۗ أَلَآ إِنَّ ٱلَّذِينَ يُمَارُونَ فِي ٱلسَّاعَةِ لَفِي ضَلَٰلِۭ بَعِيدٍ ﴾
[الشُّوري: 18]

okhawo amene sakhulupilira amafuna kuti ola lidze msanga pamene onse amene amakhulupirira amaliopa ilo chifukwa amadziwa kuti ndi loonadi. Ndithudi onse amene amakana za olali ndi otayika kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: يستعجل بها الذين لا يؤمنون بها والذين آمنوا مشفقون منها ويعلمون أنها, باللغة نيانجا

﴿يستعجل بها الذين لا يؤمنون بها والذين آمنوا مشفقون منها ويعلمون أنها﴾ [الشُّوري: 18]

Khaled Ibrahim Betala
“Akuifulumizitsa amene sakuikhulupirira; koma amene akhulupirira ali oopa za iyo, ndipo akudziwa kuti imeneyo ndiyoonadi, (za kupezeka kwake palibe chikaiko). Dziwani kuti ndithu amene akutsutsana za nthawi (ya Qiyâma) ali mkusokera konka nako kutali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek