×

Koma ngati iwo akana, Ife sitidakutumize iwe ngati owayang’anira iwo. Udindo wako 42:48 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:48) ayat 48 in Chichewa

42:48 Surah Ash-Shura ayat 48 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 48 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿فَإِنۡ أَعۡرَضُواْ فَمَآ أَرۡسَلۡنَٰكَ عَلَيۡهِمۡ حَفِيظًاۖ إِنۡ عَلَيۡكَ إِلَّا ٱلۡبَلَٰغُۗ وَإِنَّآ إِذَآ أَذَقۡنَا ٱلۡإِنسَٰنَ مِنَّا رَحۡمَةٗ فَرِحَ بِهَاۖ وَإِن تُصِبۡهُمۡ سَيِّئَةُۢ بِمَا قَدَّمَتۡ أَيۡدِيهِمۡ فَإِنَّ ٱلۡإِنسَٰنَ كَفُورٞ ﴾
[الشُّوري: 48]

Koma ngati iwo akana, Ife sitidakutumize iwe ngati owayang’anira iwo. Udindo wako ndi kungopereka uthenga. Ndipo, ndithudi, ngati Ife timupanga munthu kulawa chisomo chathu, iye amasangalala kwambiri chifukwa cha chisomocho koma ngati vuto lidza pa iwo chifukwa cha zolakwa zawo zimene adachita, ndithudi munthu amakhala osayamika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن أعرضوا فما أرسلناك عليهم حفيظا إن عليك إلا البلاغ وإنا إذا, باللغة نيانجا

﴿فإن أعرضوا فما أرسلناك عليهم حفيظا إن عليك إلا البلاغ وإنا إذا﴾ [الشُّوري: 48]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati anyalanyaza (Allah awalanga) sitidakutume kwa iwo kukhala muyang’aniri. Udindo wako ndikufalitsa uthenga. Ndipo ndithu tikamulawitsa munthu mtendere wochokera kwa Ife, akuunyadira (modzikweza), koma choipa chikawapeza kupyolera mzoipa zimene manja awo adatsogoza, pompo munthuyo sathokoza (Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek