×

Si koyenera kuti Mulungu ayankhule ndi munthu kupatula kudzera m’chivumbulutso kapena kuchokera 42:51 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:51) ayat 51 in Chichewa

42:51 Surah Ash-Shura ayat 51 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 51 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿۞ وَمَا كَانَ لِبَشَرٍ أَن يُكَلِّمَهُ ٱللَّهُ إِلَّا وَحۡيًا أَوۡ مِن وَرَآيِٕ حِجَابٍ أَوۡ يُرۡسِلَ رَسُولٗا فَيُوحِيَ بِإِذۡنِهِۦ مَا يَشَآءُۚ إِنَّهُۥ عَلِيٌّ حَكِيمٞ ﴾
[الشُّوري: 51]

Si koyenera kuti Mulungu ayankhule ndi munthu kupatula kudzera m’chivumbulutso kapena kuchokera kumalo obisika kapena potumiza Mtumwi kudzawauza, chimene Mulungu afuna ndi chilolezo chake. Ndithudi Iye ndi wapamwamba ndi wanzeru zosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان لبشر أن يكلمه الله إلا وحيا أو من وراء حجاب, باللغة نيانجا

﴿وما كان لبشر أن يكلمه الله إلا وحيا أو من وراء حجاب﴾ [الشُّوري: 51]

Khaled Ibrahim Betala
“Nkosayenera kwa munthu kuti Allah alankhule naye koma kupyolera mkumzindikiritsa, kapena kuchokera kuseri kwa chotsekereza, kapena pomtuma mtumiki (Jiburil) kuti amvumbulutsire zimene Iye akufuna mwa chilolezo Chake. Ndithu Iye Ngwapamwamba, Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek