×

Kotero, mwaulamuliro wathu, tatumiza chivumbulutso chathu kwa iwe. Iwe siumadziwa kuti chivumbulutso 42:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:52) ayat 52 in Chichewa

42:52 Surah Ash-Shura ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 52 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿وَكَذَٰلِكَ أَوۡحَيۡنَآ إِلَيۡكَ رُوحٗا مِّنۡ أَمۡرِنَاۚ مَا كُنتَ تَدۡرِي مَا ٱلۡكِتَٰبُ وَلَا ٱلۡإِيمَٰنُ وَلَٰكِن جَعَلۡنَٰهُ نُورٗا نَّهۡدِي بِهِۦ مَن نَّشَآءُ مِنۡ عِبَادِنَاۚ وَإِنَّكَ لَتَهۡدِيٓ إِلَىٰ صِرَٰطٖ مُّسۡتَقِيمٖ ﴾
[الشُّوري: 52]

Kotero, mwaulamuliro wathu, tatumiza chivumbulutso chathu kwa iwe. Iwe siumadziwa kuti chivumbulutso chidali chiyani kapena kuti chikhulupiriro chidali chiyani. Koma Ife tachipanga icho kukhala muuni umene timatsogolera nawo akapolo athu mwachifuniro chathu. Ndithudi iwe umalangiza anthu ku njira yoyenera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وكذلك أوحينا إليك روحا من أمرنا ما كنت تدري ما الكتاب ولا, باللغة نيانجا

﴿وكذلك أوحينا إليك روحا من أمرنا ما كنت تدري ما الكتاب ولا﴾ [الشُّوري: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“Momwemonso takuvumbulutsira chivumbulutso (Chathu) mwa lamulo Lathu. Siudali kudziwa kuti buku ndi chiyani, chikhulupiliro ndi chiyani; koma bukuli (Qur’an) talichita kukhala kuunika; ndi kuunikaku tikumuongola amene tam’funa mwa akapolo Athu. Ndithu iwe ukuongolera kunjira yoongoka
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek