×

Kotero tavumbulutsa kwa iwe Buku la Korani m’Chiarabu, kuti ukhoza kuchenjeza make 42:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:7) ayat 7 in Chichewa

42:7 Surah Ash-Shura ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 7 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿وَكَذَٰلِكَ أَوۡحَيۡنَآ إِلَيۡكَ قُرۡءَانًا عَرَبِيّٗا لِّتُنذِرَ أُمَّ ٱلۡقُرَىٰ وَمَنۡ حَوۡلَهَا وَتُنذِرَ يَوۡمَ ٱلۡجَمۡعِ لَا رَيۡبَ فِيهِۚ فَرِيقٞ فِي ٱلۡجَنَّةِ وَفَرِيقٞ فِي ٱلسَّعِيرِ ﴾
[الشُّوري: 7]

Kotero tavumbulutsa kwa iwe Buku la Korani m’Chiarabu, kuti ukhoza kuchenjeza make wa Mizinda ndi iyo youzungulira. Ndipo kuti uchenjeze za tsiku la chiweruzo limene mosakayika lidzadza pamene gulu lina lidzakhala ku Paradiso ndi gulu linzake lidzakhala kumoto

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وكذلك أوحينا إليك قرآنا عربيا لتنذر أم القرى ومن حولها وتنذر يوم, باللغة نيانجا

﴿وكذلك أوحينا إليك قرآنا عربيا لتنذر أم القرى ومن حولها وتنذر يوم﴾ [الشُّوري: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Chomwechonso (monga chilili chivumbulutso chapoyerachi) takuvumbulutsira Qur’an m’Chiarabu (popanda chikaiko) kuti uchenjeze (eni) manthu wa mizinda (Makka) ndi amene ali m’mbali mwake, ndikutinso uchenjeze (anthu) za tsiku la msonkhano, lopanda chikaiko. (Pa tsikulo anthu adzagawikana mmagulu awiri): gulu lina ku Jannah, ndipo gulu lina ku Moto
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek