×

Ndipo zipangizo zina zikadakhala za golide. Komabe zonsezi sizikadakhala chinthu china koma 43:35 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zukhruf ⮕ (43:35) ayat 35 in Chichewa

43:35 Surah Az-Zukhruf ayat 35 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zukhruf ayat 35 - الزُّخرُف - Page - Juz 25

﴿وَزُخۡرُفٗاۚ وَإِن كُلُّ ذَٰلِكَ لَمَّا مَتَٰعُ ٱلۡحَيَوٰةِ ٱلدُّنۡيَاۚ وَٱلۡأٓخِرَةُ عِندَ رَبِّكَ لِلۡمُتَّقِينَ ﴾
[الزُّخرُف: 35]

Ndipo zipangizo zina zikadakhala za golide. Komabe zonsezi sizikadakhala chinthu china koma chisangalalo cha m’moyo uno. Ndipo moyo umene uli nkudza, umene uli ndi Ambuye wako, ndi wa anthu ochita ntchito zabwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وزخرفا وإن كل ذلك لما متاع الحياة الدنيا والآخرة عند ربك للمتقين, باللغة نيانجا

﴿وزخرفا وإن كل ذلك لما متاع الحياة الدنيا والآخرة عند ربك للمتقين﴾ [الزُّخرُف: 35]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndiponso ndi zokongoletsa za golide. Koma zonsezo sikanthu ayi, ndi chisangalalo chabe cha dziko lapansi (chosakhalira kutha); ndipo tsiku lachimaliziro lomwe lili kwa Mbuye wako ndi la oopa Allah (potsatira malamulo Ake ndi kusiya zoletsedwa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek