×

Iwo amene sakhulupirira ndipo amaletsa anzawo kutsatira njira ya Mulungu, Iye adzasandutsa 47:1 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:1) ayat 1 in Chichewa

47:1 Surah Muhammad ayat 1 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 1 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ وَصَدُّواْ عَن سَبِيلِ ٱللَّهِ أَضَلَّ أَعۡمَٰلَهُمۡ ﴾
[مُحمد: 1]

Iwo amene sakhulupirira ndipo amaletsa anzawo kutsatira njira ya Mulungu, Iye adzasandutsa ntchito zawo kukhala zopanda pake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين كفروا وصدوا عن سبيل الله أضل أعمالهم, باللغة نيانجا

﴿الذين كفروا وصدوا عن سبيل الله أضل أعمالهم﴾ [مُحمد: 1]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene adam’kana (Allah ndi Mthenga Wake) ndi kutsekereza anthu kuyenda panjira ya Allah (powaletsa kulowa m’Chisilamu), Allah waononga zonse zabwino zimene adachita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek