×

Kodi iye amene watsogozedwa bwino ndi Ambuye wake ndi wofanana ndi iwo 47:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:14) ayat 14 in Chichewa

47:14 Surah Muhammad ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 14 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿أَفَمَن كَانَ عَلَىٰ بَيِّنَةٖ مِّن رَّبِّهِۦ كَمَن زُيِّنَ لَهُۥ سُوٓءُ عَمَلِهِۦ وَٱتَّبَعُوٓاْ أَهۡوَآءَهُم ﴾
[مُحمد: 14]

Kodi iye amene watsogozedwa bwino ndi Ambuye wake ndi wofanana ndi iwo amene ntchito zawo zoipa zimaoneka ngati zabwino ndipo amatsatira zilakolako zawo zopanda pake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفمن كان على بينة من ربه كمن زين له سوء عمله واتبعوا, باللغة نيانجا

﴿أفمن كان على بينة من ربه كمن زين له سوء عمله واتبعوا﴾ [مُحمد: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi angafanane, (polandira mphoto,) amene ali ndi umboni wodziwika wochokera kwa Mbuye wake, (kotero kuti nkumamumvera, ndi amene wakometsedwa ndi zochita zake zoipa natsatira zilakolako zawo)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek