×

Motero pamene inu mukumana ndi anthu osakhulupirira pa nkhondo, thyolani makosi awo, 47:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:4) ayat 4 in Chichewa

47:4 Surah Muhammad ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 4 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿فَإِذَا لَقِيتُمُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ فَضَرۡبَ ٱلرِّقَابِ حَتَّىٰٓ إِذَآ أَثۡخَنتُمُوهُمۡ فَشُدُّواْ ٱلۡوَثَاقَ فَإِمَّا مَنَّۢا بَعۡدُ وَإِمَّا فِدَآءً حَتَّىٰ تَضَعَ ٱلۡحَرۡبُ أَوۡزَارَهَاۚ ذَٰلِكَۖ وَلَوۡ يَشَآءُ ٱللَّهُ لَٱنتَصَرَ مِنۡهُمۡ وَلَٰكِن لِّيَبۡلُوَاْ بَعۡضَكُم بِبَعۡضٖۗ وَٱلَّذِينَ قُتِلُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ فَلَن يُضِلَّ أَعۡمَٰلَهُمۡ ﴾
[مُحمد: 4]

Motero pamene inu mukumana ndi anthu osakhulupirira pa nkhondo, thyolani makosi awo, mpaka pamene mukupha ndi kuvulaza ambiri ndipo muwagwire kukhala akaidi ndipo pambuyo pake mukhoza kuwamasula powaonetsa chisoni kapena akhale ngati chigwiriro mpaka pamene nkhondo itatha. Motero inu mwalamulidwa. Koma chikadakhala chifuniro cha Mulungu, ndithudi, Iye Mwini wake akadawapatsa chilango chowayenera. Koma Iye wafuna kuti inu mumenyane nawo ndi cholinga chokuyesani wina ndi mnzake. Koma iwo amene aphedwa m’njira ya Mulungu, Iye sadzalola kuti ntchito zawo zipite pachabe

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإذا لقيتم الذين كفروا فضرب الرقاب حتى إذا أثخنتموهم فشدوا الوثاق فإما, باللغة نيانجا

﴿فإذا لقيتم الذين كفروا فضرب الرقاب حتى إذا أثخنتموهم فشدوا الوثاق فإما﴾ [مُحمد: 4]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek