×

Si Mulunguameneadayambitsa Bahira (miyambo yosakama ngamira yaikazi kapena Saiba (ngamira yaikazi kuisiya 5:103 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:103) ayat 103 in Chichewa

5:103 Surah Al-Ma’idah ayat 103 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 103 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿مَا جَعَلَ ٱللَّهُ مِنۢ بَحِيرَةٖ وَلَا سَآئِبَةٖ وَلَا وَصِيلَةٖ وَلَا حَامٖ وَلَٰكِنَّ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ يَفۡتَرُونَ عَلَى ٱللَّهِ ٱلۡكَذِبَۖ وَأَكۡثَرُهُمۡ لَا يَعۡقِلُونَ ﴾
[المَائدة: 103]

Si Mulunguameneadayambitsa Bahira (miyambo yosakama ngamira yaikazi kapena Saiba (ngamira yaikazi kuisiya yokha kuubusa) kapena Wasila (kupereka nsembe ya nyama ya ngamila imene ibereka ana akazi motsatizana) kapena Ham (mitheno ya ngamira imene yaletsedwa kugwira ntchito) koma ndi anthu osakhulupirira amene amapeka bodza lokhudza Mulungu ndipo ambiri a iwo alibe nzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ما جعل الله من بحيرة ولا سائبة ولا وصيلة ولا حام ولكن, باللغة نيانجا

﴿ما جعل الله من بحيرة ولا سائبة ولا وصيلة ولا حام ولكن﴾ [المَائدة: 103]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah sadaike (kuletsedwa kwamtundu uliwonse) pa nyama yotchedwa Bahira*, ngakhale Saiba**, ngakhale Wasila***, ngakhalenso Hami****. Koma amene sadakhulupirire akumpekera Allah bodza. Ndipo ambiri a iwo sagwiritsa ntchito nzeru zawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek