×

Pamene zinenedwa kwa iwo kuti: Bwerani ku chimene Mulungu wavumbulutsa ndi kwa 5:104 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:104) ayat 104 in Chichewa

5:104 Surah Al-Ma’idah ayat 104 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 104 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿وَإِذَا قِيلَ لَهُمۡ تَعَالَوۡاْ إِلَىٰ مَآ أَنزَلَ ٱللَّهُ وَإِلَى ٱلرَّسُولِ قَالُواْ حَسۡبُنَا مَا وَجَدۡنَا عَلَيۡهِ ءَابَآءَنَآۚ أَوَلَوۡ كَانَ ءَابَآؤُهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ شَيۡـٔٗا وَلَا يَهۡتَدُونَ ﴾
[المَائدة: 104]

Pamene zinenedwa kwa iwo kuti: Bwerani ku chimene Mulungu wavumbulutsa ndi kwa Mtumwi. Iwo amati, “Chikhulupiriro chimene adatisiyira makolo athu ndi chotikwanira.” Ngakhale kuti makolo awo samadziwa chilichonse ndipo sadatsogozedwe bwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا قيل لهم تعالوا إلى ما أنـزل الله وإلى الرسول قالوا حسبنا, باللغة نيانجا

﴿وإذا قيل لهم تعالوا إلى ما أنـزل الله وإلى الرسول قالوا حسبنا﴾ [المَائدة: 104]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akauzidwa: “Tadzani kuchilamulo cha zomwe Allah wavumbulutsa ndi (zomwe akunena) Mtumiki.” Akunena: “Tikukwaniritsidwa ndi zomwe tidawapeza nazo makolo athu.” Kodi ngakhale kuti makolo awowo sadali kudziwa chinthu chilichonse ndipo sadali oongoka, (awatsatirabe)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek