×

Mmene ndidalamulira ophunzira ako kuti akhulupirire mwa Ine ndi mwa Mtumwi wanga, 5:111 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:111) ayat 111 in Chichewa

5:111 Surah Al-Ma’idah ayat 111 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 111 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿وَإِذۡ أَوۡحَيۡتُ إِلَى ٱلۡحَوَارِيِّـۧنَ أَنۡ ءَامِنُواْ بِي وَبِرَسُولِي قَالُوٓاْ ءَامَنَّا وَٱشۡهَدۡ بِأَنَّنَا مُسۡلِمُونَ ﴾
[المَائدة: 111]

Mmene ndidalamulira ophunzira ako kuti akhulupirire mwa Ine ndi mwa Mtumwi wanga, iwo adati: “Ife takhulupirira. Ndipo chitira umboni kuti ife tidzipereka kwathunthu kwa Mulungu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ أوحيت إلى الحواريين أن آمنوا بي وبرسولي قالوا آمنا واشهد بأننا, باللغة نيانجا

﴿وإذ أوحيت إلى الحواريين أن آمنوا بي وبرسولي قالوا آمنا واشهد بأننا﴾ [المَائدة: 111]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbukira) pamene ndidawaululira ophunzira ako kuti: “Ndikhulupirireni Ine ndi Mtumiki Wanga (uyu Isa {Yesu}).” Iwo adati: “Takhulupirira; ndipo khalani mboni kuti ife ndife Asilamu (ogonjera mwa Inu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek