×

Pamene Mulungu adzati: “O! iwe Yesu, mwana wamwamuna wa Maria! Kodi udawauza 5:116 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:116) ayat 116 in Chichewa

5:116 Surah Al-Ma’idah ayat 116 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 116 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿وَإِذۡ قَالَ ٱللَّهُ يَٰعِيسَى ٱبۡنَ مَرۡيَمَ ءَأَنتَ قُلۡتَ لِلنَّاسِ ٱتَّخِذُونِي وَأُمِّيَ إِلَٰهَيۡنِ مِن دُونِ ٱللَّهِۖ قَالَ سُبۡحَٰنَكَ مَا يَكُونُ لِيٓ أَنۡ أَقُولَ مَا لَيۡسَ لِي بِحَقٍّۚ إِن كُنتُ قُلۡتُهُۥ فَقَدۡ عَلِمۡتَهُۥۚ تَعۡلَمُ مَا فِي نَفۡسِي وَلَآ أَعۡلَمُ مَا فِي نَفۡسِكَۚ إِنَّكَ أَنتَ عَلَّٰمُ ٱلۡغُيُوبِ ﴾
[المَائدة: 116]

Pamene Mulungu adzati: “O! iwe Yesu, mwana wamwamuna wa Maria! Kodi udawauza anthu kuti: Ndipembedzeni ine ndi Amai anga ngati milungu iwiri powonjezera pa Mulungu?” Iye adzayankha: “Ulemerero ukhale kwa Inu! Sikunali koyenera kuti ine ndinene zinthu zimene ndinalibe ulamuliro wonenera. Ngati ndikadanena choncho, ndithudi, inu mukadadziwa. Inu mumadziwa zimene zili mumtima mwanga pamene ine sindidziwa zimene zili mu mtima mwanu. Inu nokha mumadziwa zinthu zobisika.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ قال الله ياعيسى ابن مريم أأنت قلت للناس اتخذوني وأمي إلهين, باللغة نيانجا

﴿وإذ قال الله ياعيسى ابن مريم أأنت قلت للناس اتخذوني وأمي إلهين﴾ [المَائدة: 116]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbukirani) pamene Allah adzanena: “Iwe Isa (Yesu) mwana wa Mariya: Kodi iwe udauza anthu kuti: ‘Ndiyeseni ine ndi mayi wanga monga milungu iwiri m’malo mwa Allah?” (Mneneri Isa {Yesu}) adzaati: “Ulemelero ukhale pa Inu. Sikoyenera kwa ine kunena zomwe sizili zoyenera (kwa ine mawu amenewa ngabodza). Ngati ndikadanena, ndiye kuti mukadadziwa. Inu mukudziwa zomwe zili mu mtima mwanga, pomwe ine sindidziwa zomwe zili mwa Inu. Ndithudi, Inu ndinu Wodziwa zamseri.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek