×

Zinthu zonse zabwino, tsiku lalero, zaloledwa kuti mukhoza kuzigwiritsa ntchito. Chakudya cha 5:5 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:5) ayat 5 in Chichewa

5:5 Surah Al-Ma’idah ayat 5 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 5 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿ٱلۡيَوۡمَ أُحِلَّ لَكُمُ ٱلطَّيِّبَٰتُۖ وَطَعَامُ ٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡكِتَٰبَ حِلّٞ لَّكُمۡ وَطَعَامُكُمۡ حِلّٞ لَّهُمۡۖ وَٱلۡمُحۡصَنَٰتُ مِنَ ٱلۡمُؤۡمِنَٰتِ وَٱلۡمُحۡصَنَٰتُ مِنَ ٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡكِتَٰبَ مِن قَبۡلِكُمۡ إِذَآ ءَاتَيۡتُمُوهُنَّ أُجُورَهُنَّ مُحۡصِنِينَ غَيۡرَ مُسَٰفِحِينَ وَلَا مُتَّخِذِيٓ أَخۡدَانٖۗ وَمَن يَكۡفُرۡ بِٱلۡإِيمَٰنِ فَقَدۡ حَبِطَ عَمَلُهُۥ وَهُوَ فِي ٱلۡأٓخِرَةِ مِنَ ٱلۡخَٰسِرِينَ ﴾
[المَائدة: 5]

Zinthu zonse zabwino, tsiku lalero, zaloledwa kuti mukhoza kuzigwiritsa ntchito. Chakudya cha anthu m’Buku ndi chololedwa kwa inu ndiponso chakudya chanu ndi chololedwa kwa iwo. Muloledwa kukwatira akazi okhulupirira ndi akazi angwiro kuchokera ku gulu la anthu a m’Buku pamene muwapatsa mphatso yawo ya ukwati ndi kukhala molemekezeka ndi iwo osachita chiwerewere kapena kuwasandutsa iwo ngati zibwenzi zanu. Ndipo aliyense amene sakhulupirira mwa Mulungu mmodzi, ntchito zake zidzakhala zopanda pake ndipo m’dziko limene lili nkudza, iye adzakhala olephera kwambiri

❮ Previous Next ❯

ترجمة: اليوم أحل لكم الطيبات وطعام الذين أوتوا الكتاب حل لكم وطعامكم حل, باللغة نيانجا

﴿اليوم أحل لكم الطيبات وطعام الذين أوتوا الكتاب حل لكم وطعامكم حل﴾ [المَائدة: 5]

Khaled Ibrahim Betala
“Lero mwaloledwa zonse zabwino ndi chakudya cha omwe adapatsidwa buku nchololedwa kwa inu, ndiponso chakudya chanu nchololedwa kwa iwo, ndipo (mukuloledwa kuwakwatira) akazi abwino a mwa okhulupirira ndi akazi abwino a mwa omwe adapatsidwa ma buku kale, ngati mwawapatsa chiwongo chawo m’njira yomanga nawo ukwati, osati mochita nao chiwerewere, osatinso mochita nao zibwenzi. Ndipo amene akane kukhulupirira, ndiye kuti yaonongeka ntchito yake; ndipo iye tsiku lachimaliziro adzakhala mwa oluza (otaiyika)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek