×

Oh inu anthu okhulupirira! Pamene mukonzeka kuti mupemphere, sambitsani nkhope zanu ndiponso 5:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:6) ayat 6 in Chichewa

5:6 Surah Al-Ma’idah ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 6 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ إِذَا قُمۡتُمۡ إِلَى ٱلصَّلَوٰةِ فَٱغۡسِلُواْ وُجُوهَكُمۡ وَأَيۡدِيَكُمۡ إِلَى ٱلۡمَرَافِقِ وَٱمۡسَحُواْ بِرُءُوسِكُمۡ وَأَرۡجُلَكُمۡ إِلَى ٱلۡكَعۡبَيۡنِۚ وَإِن كُنتُمۡ جُنُبٗا فَٱطَّهَّرُواْۚ وَإِن كُنتُم مَّرۡضَىٰٓ أَوۡ عَلَىٰ سَفَرٍ أَوۡ جَآءَ أَحَدٞ مِّنكُم مِّنَ ٱلۡغَآئِطِ أَوۡ لَٰمَسۡتُمُ ٱلنِّسَآءَ فَلَمۡ تَجِدُواْ مَآءٗ فَتَيَمَّمُواْ صَعِيدٗا طَيِّبٗا فَٱمۡسَحُواْ بِوُجُوهِكُمۡ وَأَيۡدِيكُم مِّنۡهُۚ مَا يُرِيدُ ٱللَّهُ لِيَجۡعَلَ عَلَيۡكُم مِّنۡ حَرَجٖ وَلَٰكِن يُرِيدُ لِيُطَهِّرَكُمۡ وَلِيُتِمَّ نِعۡمَتَهُۥ عَلَيۡكُمۡ لَعَلَّكُمۡ تَشۡكُرُونَ ﴾
[المَائدة: 6]

Oh inu anthu okhulupirira! Pamene mukonzeka kuti mupemphere, sambitsani nkhope zanu ndiponso manja anu mpaka pa kasukusuku ndipo pakani ku mutu kwanu ndipo sambitsani mapazi anu mpaka molekezera phazi lanu. Ngati mwadetsedwa, dziyeretseni. Koma ngati muli kudwala kapena muli paulendo, kapena wina wa inu abwera kuchokera ku chimbudzi kapena munagona ndi akazi anu ndipo mwasowa madzi, tengani mchenga woyera ndi kupukuta m’manja mwanu ndi ku nkhope kwanu. Mulungu safuna kukukundikirani mtolo wolemera koma Iye afuna kukuyeretsani ndi kukwaniritsa zokoma zake kwa inu kuti inu mukhale oyamika

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا إذا قمتم إلى الصلاة فاغسلوا وجوهكم وأيديكم إلى المرافق, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا إذا قمتم إلى الصلاة فاغسلوا وجوهكم وأيديكم إلى المرافق﴾ [المَائدة: 6]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek