×

Ayudaamanenakuti:“Manjaa Mulungundiomangika.” Manja awo ndiwo akhale omangika ndiponso iwo atembereredwe chifukwa cha 5:64 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:64) ayat 64 in Chichewa

5:64 Surah Al-Ma’idah ayat 64 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 64 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَقَالَتِ ٱلۡيَهُودُ يَدُ ٱللَّهِ مَغۡلُولَةٌۚ غُلَّتۡ أَيۡدِيهِمۡ وَلُعِنُواْ بِمَا قَالُواْۘ بَلۡ يَدَاهُ مَبۡسُوطَتَانِ يُنفِقُ كَيۡفَ يَشَآءُۚ وَلَيَزِيدَنَّ كَثِيرٗا مِّنۡهُم مَّآ أُنزِلَ إِلَيۡكَ مِن رَّبِّكَ طُغۡيَٰنٗا وَكُفۡرٗاۚ وَأَلۡقَيۡنَا بَيۡنَهُمُ ٱلۡعَدَٰوَةَ وَٱلۡبَغۡضَآءَ إِلَىٰ يَوۡمِ ٱلۡقِيَٰمَةِۚ كُلَّمَآ أَوۡقَدُواْ نَارٗا لِّلۡحَرۡبِ أَطۡفَأَهَا ٱللَّهُۚ وَيَسۡعَوۡنَ فِي ٱلۡأَرۡضِ فَسَادٗاۚ وَٱللَّهُ لَا يُحِبُّ ٱلۡمُفۡسِدِينَ ﴾
[المَائدة: 64]

Ayudaamanenakuti:“Manjaa Mulungundiomangika.” Manja awo ndiwo akhale omangika ndiponso iwo atembereredwe chifukwa cha zimene anena! Iyayi! Manja onse a Mulungu ndi otambasuka. Iye amapereka mmene wafunira. Ndithudi chimene Mulungu wavumbulutsa kwa iwe chimaonjezera udani ndi kusakhulupirira kwa anthu ambiri mwaiwo. Ife taika pakati pawo ndi kukhazikitsa udani mpaka patsiku louka kwa akufa. Nthawi zonse pamene iwo ayatsa moto wa nkhondo, Mulungu amauzima ndipo iwo amayesetsa kupanga zoipa padziko. Mulungu sakonda anthu oyambitsa chisokonezo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وقالت اليهود يد الله مغلولة غلت أيديهم ولعنوا بما قالوا بل يداه, باللغة نيانجا

﴿وقالت اليهود يد الله مغلولة غلت أيديهم ولعنوا بما قالوا بل يداه﴾ [المَائدة: 64]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Ayuda adati: “Dzanja la Allah lafumbatika (sitikupeza chuma ngati kale). (Koma sichoncho); manja awo ndiwo afumbatika (posachita zabwino ndi kuchenjelera anthu). Ndipo atembeleredwa chifukwa cha zomwe anena. Koma manja ake (Allah) ngotambasuka. Amapatsa mmene wafunira. Ndithudi, zimene zavumbulutsidwa kwa iwe kuchokera kwa Mbuye wako, ziwaonjezera ambiri a iwo (Ayuda) kulumpha malire ndi kusakhulupirira. Ndipo taika chidani ndi kusakondana pakati pawo mpaka tsiku la chimariziro. Nthawi iliyonse akayatsa moto wa nkhondo, Allah amauzimitsa. Ndipo amayesetsa kudzetsa chisokonezo pa dziko, (koma Allah sawathandiza). Ndipo Allah sakonda owononga
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek