×

oh inu anthu okhulupirira! Limbikirani chifukwa cha Mulungu ndipo perekani umboni woona 5:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:8) ayat 8 in Chichewa

5:8 Surah Al-Ma’idah ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 8 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ كُونُواْ قَوَّٰمِينَ لِلَّهِ شُهَدَآءَ بِٱلۡقِسۡطِۖ وَلَا يَجۡرِمَنَّكُمۡ شَنَـَٔانُ قَوۡمٍ عَلَىٰٓ أَلَّا تَعۡدِلُواْۚ ٱعۡدِلُواْ هُوَ أَقۡرَبُ لِلتَّقۡوَىٰۖ وَٱتَّقُواْ ٱللَّهَۚ إِنَّ ٱللَّهَ خَبِيرُۢ بِمَا تَعۡمَلُونَ ﴾
[المَائدة: 8]

oh inu anthu okhulupirira! Limbikirani chifukwa cha Mulungu ndipo perekani umboni woona wokhawokha ndipo musalole chidani chimene chilipo ndi anthu ena kuti chikusokonezeni kuchita chilungamo. Chitani chilungamo chifukwa chilungamo chili kufupi ndi kuyera mtima ndipo opani Mulungu. Ndithudi Mulungu amadziwa ntchito zonsezimenemumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا كونوا قوامين لله شهداء بالقسط ولا يجرمنكم شنآن قوم, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا كونوا قوامين لله شهداء بالقسط ولا يجرمنكم شنآن قوم﴾ [المَائدة: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Khalani olungama kwa Allah, opereka umboni mwachilungamo, ndipo chidani cha anthu pa inu chisakuchititseni kuti musachite chilungamo. Chitani chilungamo; kutero kumakuyandikitsani ku “taquwa” (kuopa Allah). Ndipo opani Allah. Ndithudi, Allah Ngodziwa nkhani zonse za (zinthu) zomwe muchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek