×

Ndithudi tidatumiza kale Atumwi athu ndi zizindikiro zooneka ndipo tidatumiza pamodzi ndi 57:25 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:25) ayat 25 in Chichewa

57:25 Surah Al-hadid ayat 25 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 25 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿لَقَدۡ أَرۡسَلۡنَا رُسُلَنَا بِٱلۡبَيِّنَٰتِ وَأَنزَلۡنَا مَعَهُمُ ٱلۡكِتَٰبَ وَٱلۡمِيزَانَ لِيَقُومَ ٱلنَّاسُ بِٱلۡقِسۡطِۖ وَأَنزَلۡنَا ٱلۡحَدِيدَ فِيهِ بَأۡسٞ شَدِيدٞ وَمَنَٰفِعُ لِلنَّاسِ وَلِيَعۡلَمَ ٱللَّهُ مَن يَنصُرُهُۥ وَرُسُلَهُۥ بِٱلۡغَيۡبِۚ إِنَّ ٱللَّهَ قَوِيٌّ عَزِيزٞ ﴾
[الحدِيد: 25]

Ndithudi tidatumiza kale Atumwi athu ndi zizindikiro zooneka ndipo tidatumiza pamodzi ndi iwo Buku ndi muyeso kuti anthu akhoza kukhala ndi makhalidwe abwino. Ndipo Ife tidapanga chitsulo chimene m’kati mwake muli mphamvu ndi zinthu zambiri zabwino kwa anthu. Kuti Mulungu akhoza kuyesa iwo amene amamuthandiza Iye ndi Mtumwi wake mwamseri. Ndithudi Mulungu ndi wolimba ndi wamphamvu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لقد أرسلنا رسلنا بالبينات وأنـزلنا معهم الكتاب والميزان ليقوم الناس بالقسط وأنـزلنا, باللغة نيانجا

﴿لقد أرسلنا رسلنا بالبينات وأنـزلنا معهم الكتاب والميزان ليقوم الناس بالقسط وأنـزلنا﴾ [الحدِيد: 25]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek