×

Ndiponso anthu a umbombo amauza anzawo kuti nawonso azikhala a umbombo. Ngati 57:24 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:24) ayat 24 in Chichewa

57:24 Surah Al-hadid ayat 24 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 24 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿ٱلَّذِينَ يَبۡخَلُونَ وَيَأۡمُرُونَ ٱلنَّاسَ بِٱلۡبُخۡلِۗ وَمَن يَتَوَلَّ فَإِنَّ ٱللَّهَ هُوَ ٱلۡغَنِيُّ ٱلۡحَمِيدُ ﴾
[الحدِيد: 24]

Ndiponso anthu a umbombo amauza anzawo kuti nawonso azikhala a umbombo. Ngati wina abwerera m’mbuyo kuchokera ku njira ya Mulungu, ndithudi, Mulungu sasowa chilichonse ndipo ndi wolemekezeka

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين يبخلون ويأمرون الناس بالبخل ومن يتول فإن الله هو الغني الحميد, باللغة نيانجا

﴿الذين يبخلون ويأمرون الناس بالبخل ومن يتول فإن الله هو الغني الحميد﴾ [الحدِيد: 24]

Khaled Ibrahim Betala
“Amene akuchita umbombo (ndi chuma chawo; ndipo osapereka pa njira ya Allah) ndi kumalamula anthu ena kuchita umbombo. Ndipo amene atembenuke (adzalandira chilango chachikulu), ndithu Allah Ngolemera, (sasaukira chilichonse kwa wina), Ngotamandidwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek