×

Khulupirirani mwa Mulungu ndi Mtumwi wake. Perekani zopereka zaulere kuchokera ku zinthu 57:7 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:7) ayat 7 in Chichewa

57:7 Surah Al-hadid ayat 7 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 7 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿ءَامِنُواْ بِٱللَّهِ وَرَسُولِهِۦ وَأَنفِقُواْ مِمَّا جَعَلَكُم مُّسۡتَخۡلَفِينَ فِيهِۖ فَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ مِنكُمۡ وَأَنفَقُواْ لَهُمۡ أَجۡرٞ كَبِيرٞ ﴾
[الحدِيد: 7]

Khulupirirani mwa Mulungu ndi Mtumwi wake. Perekani zopereka zaulere kuchokera ku zinthu zimene Mulungu wakupatsani kuti zikhale zanu. Iwo a inu amene akhulupilira ndipo apereka chaulere, yawo idzakhala mphotho yaikulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: آمنوا بالله ورسوله وأنفقوا مما جعلكم مستخلفين فيه فالذين آمنوا منكم وأنفقوا, باللغة نيانجا

﴿آمنوا بالله ورسوله وأنفقوا مما جعلكم مستخلفين فيه فالذين آمنوا منكم وأنفقوا﴾ [الحدِيد: 7]

Khaled Ibrahim Betala
“Khulupirirani Allah ndi Mthenga Wake, ndipo perekani (pa njira ya Allah m’chuma chimene Allah wakupatsani uchiyang’anira. Choncho mwa inu amene akhulupirira (mwa Allah ndi mthenga Wake) ndikupereka (zimene awapatsa) iwo ali ndi malipiro aakulu (kwa Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek