×

Kodi ndi chifukwa chiyani kuti inu simukhulupirira mwa Mulungu? Pamene Mtumwi ali 57:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:8) ayat 8 in Chichewa

57:8 Surah Al-hadid ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 8 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿وَمَا لَكُمۡ لَا تُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلرَّسُولُ يَدۡعُوكُمۡ لِتُؤۡمِنُواْ بِرَبِّكُمۡ وَقَدۡ أَخَذَ مِيثَٰقَكُمۡ إِن كُنتُم مُّؤۡمِنِينَ ﴾
[الحدِيد: 8]

Kodi ndi chifukwa chiyani kuti inu simukhulupirira mwa Mulungu? Pamene Mtumwi ali kukuitanani kuti mukhulupirire mwa Ambuye wanu ndipo Iye, ndithudi, walandira lonjezo lanu ngati inu ndinu anthu okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما لكم لا تؤمنون بالله والرسول يدعوكم لتؤمنوا بربكم وقد أخذ ميثاقكم, باللغة نيانجا

﴿وما لكم لا تؤمنون بالله والرسول يدعوكم لتؤمنوا بربكم وقد أخذ ميثاقكم﴾ [الحدِيد: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi nchifukwa ninji simukhulupirira Allah pomwe Mtumiki akukuitanani kuti mukhulupirire Mbuye wanu (ndi kukulimbitsani pa zimenezo) chikhalirecho (Iye) adalandira lonjezo lanu, (muli mumsana wa tate wanu Adam kuti mdzakhulupirira,) ngati mulidi okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek