×

Iwe sudzapeza anthu amene amakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza ali kuchita 58:22 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mujadilah ⮕ (58:22) ayat 22 in Chichewa

58:22 Surah Al-Mujadilah ayat 22 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mujadilah ayat 22 - المُجَادلة - Page - Juz 28

﴿لَّا تَجِدُ قَوۡمٗا يُؤۡمِنُونَ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِ يُوَآدُّونَ مَنۡ حَآدَّ ٱللَّهَ وَرَسُولَهُۥ وَلَوۡ كَانُوٓاْ ءَابَآءَهُمۡ أَوۡ أَبۡنَآءَهُمۡ أَوۡ إِخۡوَٰنَهُمۡ أَوۡ عَشِيرَتَهُمۡۚ أُوْلَٰٓئِكَ كَتَبَ فِي قُلُوبِهِمُ ٱلۡإِيمَٰنَ وَأَيَّدَهُم بِرُوحٖ مِّنۡهُۖ وَيُدۡخِلُهُمۡ جَنَّٰتٖ تَجۡرِي مِن تَحۡتِهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَاۚ رَضِيَ ٱللَّهُ عَنۡهُمۡ وَرَضُواْ عَنۡهُۚ أُوْلَٰٓئِكَ حِزۡبُ ٱللَّهِۚ أَلَآ إِنَّ حِزۡبَ ٱللَّهِ هُمُ ٱلۡمُفۡلِحُونَ ﴾
[المُجَادلة: 22]

Iwe sudzapeza anthu amene amakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza ali kuchita chibwenzi ndi iwo amene amatsutsa Mulungu ndi Mtumwi wake ngakhale kuti atakhala abambo wawo, kapena ana awo kapena abale awo kapena anansi awo. Kwa awa, Iye wakhazikitsa chikhulupiriro m’mitima mwawo, ndipo wawalimbikitsa ndi ulangizi, wochokera kwa Iye. Ndipo Iye adzawalandira m’minda ya Paradiso, imene pansi pake pamayenda mitsinje kuti akhale komweko mpaka kalekale. Mulungu wasangalala nawo ndipo nawonso asangalala ndi Iye. Iwo ndi anthu a gulu la Mulungu. Ndithudi ndi anthu a Mulungu amene adzapambana

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا تجد قوما يؤمنون بالله واليوم الآخر يوادون من حاد الله ورسوله, باللغة نيانجا

﴿لا تجد قوما يؤمنون بالله واليوم الآخر يوادون من حاد الله ورسوله﴾ [المُجَادلة: 22]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek