×

Koma pamene zabwino zinali kudza kwa iwo, iwo amati: “Zimenezi ndi zotiyenera.” 7:131 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:131) ayat 131 in Chichewa

7:131 Surah Al-A‘raf ayat 131 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 131 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿فَإِذَا جَآءَتۡهُمُ ٱلۡحَسَنَةُ قَالُواْ لَنَا هَٰذِهِۦۖ وَإِن تُصِبۡهُمۡ سَيِّئَةٞ يَطَّيَّرُواْ بِمُوسَىٰ وَمَن مَّعَهُۥٓۗ أَلَآ إِنَّمَا طَٰٓئِرُهُمۡ عِندَ ٱللَّهِ وَلَٰكِنَّ أَكۡثَرَهُمۡ لَا يَعۡلَمُونَ ﴾
[الأعرَاف: 131]

Koma pamene zabwino zinali kudza kwa iwo, iwo amati: “Zimenezi ndi zotiyenera.” Koma ngati choipa chimadza pa iwo, adali kunena kuti chadza chifukwa cha Mose ndi anthu ake. Dziwani! Ndithudi zoipa zawo zimachokera kwa Mulungu koma ambiri a iwo sadziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإذا جاءتهم الحسنة قالوا لنا هذه وإن تصبهم سيئة يطيروا بموسى ومن, باللغة نيانجا

﴿فإذا جاءتهم الحسنة قالوا لنا هذه وإن تصبهم سيئة يطيروا بموسى ومن﴾ [الأعرَاف: 131]

Khaled Ibrahim Betala
“(Adali chonchi): Ubwino ukawadzera, amati: “Ubwinowu nchifukwa cha zochita zathu zabwino.” Ndipo choipa chikawadzera, amakankhira kwa Mûsa ndi amene adali naye. (Amati iye ndiye wadzetsa tsokalo chifukwa choisambula milungu yawo). Dziwani kuti tsoka lawo limachokera kwa Allah (chifukwa cha zochita zawo zoipa). Koma ambiri a iwo sazindikira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek