×

Motero ife tidawatumizira chigumula ndi dzombe, nsabwe, achule, ndi magazi kukhala zizindikiro 7:133 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:133) ayat 133 in Chichewa

7:133 Surah Al-A‘raf ayat 133 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 133 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿فَأَرۡسَلۡنَا عَلَيۡهِمُ ٱلطُّوفَانَ وَٱلۡجَرَادَ وَٱلۡقُمَّلَ وَٱلضَّفَادِعَ وَٱلدَّمَ ءَايَٰتٖ مُّفَصَّلَٰتٖ فَٱسۡتَكۡبَرُواْ وَكَانُواْ قَوۡمٗا مُّجۡرِمِينَ ﴾
[الأعرَاف: 133]

Motero ife tidawatumizira chigumula ndi dzombe, nsabwe, achule, ndi magazi kukhala zizindikiro zoonadi zosiyanasiyana zooneka komabe iwo adazikana izo chifukwa chakuti adali anthu ochimwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فأرسلنا عليهم الطوفان والجراد والقمل والضفادع والدم آيات مفصلات فاستكبروا وكانوا قوما, باللغة نيانجا

﴿فأرسلنا عليهم الطوفان والجراد والقمل والضفادع والدم آيات مفصلات فاستكبروا وكانوا قوما﴾ [الأعرَاف: 133]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, tidawatumizira chigumula, (mliri wa) dzombe, nsabwe, achule ndi magazi monga zizindikiro zosiyanasiyana. Koma adadzikuza; ndipo adali anthu oipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek