×

Ife tidamusankhira Mose masiku makumi atatu ndipo tinaonjeza masiku khumi ena, motero 7:142 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:142) ayat 142 in Chichewa

7:142 Surah Al-A‘raf ayat 142 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 142 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿۞ وَوَٰعَدۡنَا مُوسَىٰ ثَلَٰثِينَ لَيۡلَةٗ وَأَتۡمَمۡنَٰهَا بِعَشۡرٖ فَتَمَّ مِيقَٰتُ رَبِّهِۦٓ أَرۡبَعِينَ لَيۡلَةٗۚ وَقَالَ مُوسَىٰ لِأَخِيهِ هَٰرُونَ ٱخۡلُفۡنِي فِي قَوۡمِي وَأَصۡلِحۡ وَلَا تَتَّبِعۡ سَبِيلَ ٱلۡمُفۡسِدِينَ ﴾
[الأعرَاف: 142]

Ife tidamusankhira Mose masiku makumi atatu ndipo tinaonjeza masiku khumi ena, motero iye adakwaniritsa nthawi imene adasankhidwa ndi Ambuye wake ya masiku makumi anayi ndipo Mose anamuuza m’bale wake Aroni kuti: Lowa m’malo mwanga pakati pa anthu anga. Uchite zinthu za ngwiro ndipo usatsatire njira ya anthu ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وواعدنا موسى ثلاثين ليلة وأتممناها بعشر فتم ميقات ربه أربعين ليلة وقال, باللغة نيانجا

﴿وواعدنا موسى ثلاثين ليلة وأتممناها بعشر فتم ميقات ربه أربعين ليلة وقال﴾ [الأعرَاف: 142]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo tidamlonjeza Mûsa masiku makumi atatu (kuti achite mapemphero kuti kenako timpatse Taurat). Ndipo tidawakwaniritsa ndi masiku khumi; chomwecho lidakwanira pangano la Mbuye wake (lopita kukampatsa Tauratiyo) m’masiku makumi anayi. Ndipo Mûsa adati kwa m’bale wake Harun: “Lowa m’malo mwanga pa (kuwatsogolera) anthu angawa. Ndipo konza; usatsate njira ya oononga.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek