×

Kodi iwo sayang’ana mu Ufumu wa kumwamba ndi wa dziko lapansi ndi 7:185 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:185) ayat 185 in Chichewa

7:185 Surah Al-A‘raf ayat 185 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 185 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿أَوَلَمۡ يَنظُرُواْ فِي مَلَكُوتِ ٱلسَّمَٰوَٰتِ وَٱلۡأَرۡضِ وَمَا خَلَقَ ٱللَّهُ مِن شَيۡءٖ وَأَنۡ عَسَىٰٓ أَن يَكُونَ قَدِ ٱقۡتَرَبَ أَجَلُهُمۡۖ فَبِأَيِّ حَدِيثِۭ بَعۡدَهُۥ يُؤۡمِنُونَ ﴾
[الأعرَاف: 185]

Kodi iwo sayang’ana mu Ufumu wa kumwamba ndi wa dziko lapansi ndi zonse zimene Mulungu adazilenga kuti aone ngati ndi mapeto a moyo wawo? Kodi ndi uthenga uti pambuyo pa uwu umene iwo adzakhulupirire

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أو لم ينظروا في ملكوت السموات والأرض وما خلق الله من شيء, باللغة نيانجا

﴿أو لم ينظروا في ملكوت السموات والأرض وما خلق الله من شيء﴾ [الأعرَاف: 185]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi saona ufumu wa kumwamba ndi pansi, ndi zinthu zomwe Allah adalenga? Mwina mwake nthawi yawo yofera yayandikira. (Nanga adzalingalira liti zolengedwa za Allah)? Kodi ndi nkhani iti pambuyo pa iyi (Qur’an) imene adzaikhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek