×

Ndipo pakati pawo padzakhala chotchinga ndi chipupa mmene mudzakhala anthu amene adzazindikira 7:46 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:46) ayat 46 in Chichewa

7:46 Surah Al-A‘raf ayat 46 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 46 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَبَيۡنَهُمَا حِجَابٞۚ وَعَلَى ٱلۡأَعۡرَافِ رِجَالٞ يَعۡرِفُونَ كُلَّۢا بِسِيمَىٰهُمۡۚ وَنَادَوۡاْ أَصۡحَٰبَ ٱلۡجَنَّةِ أَن سَلَٰمٌ عَلَيۡكُمۡۚ لَمۡ يَدۡخُلُوهَا وَهُمۡ يَطۡمَعُونَ ﴾
[الأعرَاف: 46]

Ndipo pakati pawo padzakhala chotchinga ndi chipupa mmene mudzakhala anthu amene adzazindikira wina aliyense poona zizindikiro zawo. Iwo adzaitana anthu a ku Paradiso: Mtendere ukhale pa inu. Koma panthawi imeneyo iwo adzakhala asadalowe ku Paradiso koma iwo adzakhala ndi chikhulupiriro choti adzalowanso mopanda chikaiko

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وبينهما حجاب وعلى الأعراف رجال يعرفون كلا بسيماهم ونادوا أصحاب الجنة أن, باللغة نيانجا

﴿وبينهما حجاب وعلى الأعراف رجال يعرفون كلا بسيماهم ونادوا أصحاب الجنة أن﴾ [الأعرَاف: 46]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo pakati pawo (pa anthu a ku Munda wamtendere ndi a ku Moto) padzakhala chotchinga. Ndipo pamwamba pachikweza padzakhala anthu ena (ofanana ntchito zawo zabwino ndi zoyipa) omwe akazindikira onse (a ku Jannah ndi ku Moto), ndi zizindikiro zawo. Ndipo akawaitana anthu a ku Jannah (kuti): “Salaamun Alayikum (mtendere ukhale pa inu).” Koma asanailowe uku ali ndi chikhulupiliro (kuti ailowa)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek