×

Iye ndi amene amatumiza mphepo ngati yobweretsa uthenga wabwino umene umadza pambuyo 7:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:57) ayat 57 in Chichewa

7:57 Surah Al-A‘raf ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 57 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَهُوَ ٱلَّذِي يُرۡسِلُ ٱلرِّيَٰحَ بُشۡرَۢا بَيۡنَ يَدَيۡ رَحۡمَتِهِۦۖ حَتَّىٰٓ إِذَآ أَقَلَّتۡ سَحَابٗا ثِقَالٗا سُقۡنَٰهُ لِبَلَدٖ مَّيِّتٖ فَأَنزَلۡنَا بِهِ ٱلۡمَآءَ فَأَخۡرَجۡنَا بِهِۦ مِن كُلِّ ٱلثَّمَرَٰتِۚ كَذَٰلِكَ نُخۡرِجُ ٱلۡمَوۡتَىٰ لَعَلَّكُمۡ تَذَكَّرُونَ ﴾
[الأعرَاف: 57]

Iye ndi amene amatumiza mphepo ngati yobweretsa uthenga wabwino umene umadza pambuyo pa chisomo chake. Mpaka pamene iyo isonkhanitsa mitambo yolemera, timaiyendetsa kupita ku nthaka yakufa ndipo timatumiza mvula kuti igwe pa iyo. Ndipo timameretsa zipatso za mitundu mitundu. Mmenemu ndi mmene tidzadzutsire anthu akufa kuti mwina mukhoza ku chenjezedwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وهو الذي يرسل الرياح بشرا بين يدي رحمته حتى إذا أقلت سحابا, باللغة نيانجا

﴿وهو الذي يرسل الرياح بشرا بين يدي رحمته حتى إذا أقلت سحابا﴾ [الأعرَاف: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Iye ndi Yemwe amatumiza mphepo kuti ikhale nkhani yosangalatsa patsogolo pa chifundo Chake (mvula), kufikira mphepoyo itasenza mitambo yolemera yomwe tikuitumiza ku dziko lakufa. Ndipo kupyolera mwa iyo tikutsitsa madzi ndipo ndimadzio tikutulutsa mitundu yonse ya zipatso. Momwemo ndimo tidzawaukitsira akufa. (Zonsezi) nkuti inu mukumbukire
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek