×

Nthaka yabwino imabereka zipatso mwachifuniro cha Mulungu. Nthaka yoipa siibereka chilichonse pokhapokha 7:58 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:58) ayat 58 in Chichewa

7:58 Surah Al-A‘raf ayat 58 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 58 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَٱلۡبَلَدُ ٱلطَّيِّبُ يَخۡرُجُ نَبَاتُهُۥ بِإِذۡنِ رَبِّهِۦۖ وَٱلَّذِي خَبُثَ لَا يَخۡرُجُ إِلَّا نَكِدٗاۚ كَذَٰلِكَ نُصَرِّفُ ٱلۡأٓيَٰتِ لِقَوۡمٖ يَشۡكُرُونَ ﴾
[الأعرَاف: 58]

Nthaka yabwino imabereka zipatso mwachifuniro cha Mulungu. Nthaka yoipa siibereka chilichonse pokhapokha movutikira. Motero timafotokoza zivumbulutso zathu poyera kwa anthu amene amathokoza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والبلد الطيب يخرج نباته بإذن ربه والذي خبث لا يخرج إلا نكدا, باللغة نيانجا

﴿والبلد الطيب يخرج نباته بإذن ربه والذي خبث لا يخرج إلا نكدا﴾ [الأعرَاف: 58]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo m’nthaka yabwino umatuluka mmera wake (mwachangu) mwachilolezo cha Mbuye wake. Ndipo nthaka yomwe ili yoipa siitulutsa (mmera wake) koma movutikira. M’menemo ndi momwe Tikuchifotokozera chivumbulutso momveka kwa anthu oyamika
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek