×

Mulungu anafuna kukusangalatsani chabe kuti mitima yanu ikhazikike. Ndipo palibe kupambana kupatula 8:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:10) ayat 10 in Chichewa

8:10 Surah Al-Anfal ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 10 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿وَمَا جَعَلَهُ ٱللَّهُ إِلَّا بُشۡرَىٰ وَلِتَطۡمَئِنَّ بِهِۦ قُلُوبُكُمۡۚ وَمَا ٱلنَّصۡرُ إِلَّا مِنۡ عِندِ ٱللَّهِۚ إِنَّ ٱللَّهَ عَزِيزٌ حَكِيمٌ ﴾
[الأنفَال: 10]

Mulungu anafuna kukusangalatsani chabe kuti mitima yanu ikhazikike. Ndipo palibe kupambana kupatula kochokera kwa Mulungu. Ndithudi Mulungu ndi Wamphamvu ndi Wanzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما جعله الله إلا بشرى ولتطمئن به قلوبكم وما النصر إلا من, باللغة نيانجا

﴿وما جعله الله إلا بشرى ولتطمئن به قلوبكم وما النصر إلا من﴾ [الأنفَال: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah sadachite ichi koma kuti chikhale nkhani yabwino (yosangalatsa), ndi kuti mitima yanu ikhazikike ndi chimenecho. Ndipo palibe chipulumutso (chothandiza) koma chimene chachokera kwa Allah. Ndithu Allah Ngwamphamvu zoposa, Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek