×

Ndi pamene inu mudapempha thandizo la Ambuye wanu ndipo Iye adakuyankhani: “Ine 8:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:9) ayat 9 in Chichewa

8:9 Surah Al-Anfal ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 9 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿إِذۡ تَسۡتَغِيثُونَ رَبَّكُمۡ فَٱسۡتَجَابَ لَكُمۡ أَنِّي مُمِدُّكُم بِأَلۡفٖ مِّنَ ٱلۡمَلَٰٓئِكَةِ مُرۡدِفِينَ ﴾
[الأنفَال: 9]

Ndi pamene inu mudapempha thandizo la Ambuye wanu ndipo Iye adakuyankhani: “Ine ndikuthandizani ndi angelo chikwi chimodzi m’magulumagulu otsatana.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ تستغيثون ربكم فاستجاب لكم أني ممدكم بألف من الملائكة مردفين, باللغة نيانجا

﴿إذ تستغيثون ربكم فاستجاب لكم أني ممدكم بألف من الملائكة مردفين﴾ [الأنفَال: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukirani) pamene mudali kupempha Mbuye wanu chithandizo, ndipo anakuyankhani kuti: “Ndithudi, Ine ndikuthandizani ndi chikwi cha angelo otsatizana potsika, (omenya nkhondo).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek