×

Pamene adakubweretsani inu tulo ngati mtendere kuchokera kwa Iye ndipo adakutumizirani mvula 8:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:11) ayat 11 in Chichewa

8:11 Surah Al-Anfal ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 11 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿إِذۡ يُغَشِّيكُمُ ٱلنُّعَاسَ أَمَنَةٗ مِّنۡهُ وَيُنَزِّلُ عَلَيۡكُم مِّنَ ٱلسَّمَآءِ مَآءٗ لِّيُطَهِّرَكُم بِهِۦ وَيُذۡهِبَ عَنكُمۡ رِجۡزَ ٱلشَّيۡطَٰنِ وَلِيَرۡبِطَ عَلَىٰ قُلُوبِكُمۡ وَيُثَبِّتَ بِهِ ٱلۡأَقۡدَامَ ﴾
[الأنفَال: 11]

Pamene adakubweretsani inu tulo ngati mtendere kuchokera kwa Iye ndipo adakutumizirani mvula kuchokera kumwamba kuti ikutsukeni ndi kukuyeretsani ku uve wa Satana ndi kulimbikitsa mitima yanu ndi mapazi anu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ يغشيكم النعاس أمنة منه وينـزل عليكم من السماء ماء ليطهركم به, باللغة نيانجا

﴿إذ يغشيكم النعاس أمنة منه وينـزل عليكم من السماء ماء ليطهركم به﴾ [الأنفَال: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukirani) pamene anakugonetsani tulo tomwe tidali mtendere wochokera kwa Iye, ndipo anavumbwitsa mvula pa inu yochokera ku mitambo kuti akuyeretseni nayo (matupi anu) ndikukuchotserani manong’onong’o a satana, ndi kuipatsa mphamvu mitima yanu ndiponso ndi kulimbikitsa mapazi anu (pamchenga)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek