×

Inu simunawaphe ai koma Mulungu ndiye amene anawapha. Iwe siudaponye pamene udaponya 8:17 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:17) ayat 17 in Chichewa

8:17 Surah Al-Anfal ayat 17 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 17 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿فَلَمۡ تَقۡتُلُوهُمۡ وَلَٰكِنَّ ٱللَّهَ قَتَلَهُمۡۚ وَمَا رَمَيۡتَ إِذۡ رَمَيۡتَ وَلَٰكِنَّ ٱللَّهَ رَمَىٰ وَلِيُبۡلِيَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ مِنۡهُ بَلَآءً حَسَنًاۚ إِنَّ ٱللَّهَ سَمِيعٌ عَلِيمٞ ﴾
[الأنفَال: 17]

Inu simunawaphe ai koma Mulungu ndiye amene anawapha. Iwe siudaponye pamene udaponya koma Mulungu ndi amene adaponya kuti akhoza kuyesa okhulupirira ndi mayesero oyenera ochokera kwa Iye. Ndithudi Mulungu ndi wakumva ndi wodziwa chili chonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلم تقتلوهم ولكن الله قتلهم وما رميت إذ رميت ولكن الله رمى, باللغة نيانجا

﴿فلم تقتلوهم ولكن الله قتلهم وما رميت إذ رميت ولكن الله رمى﴾ [الأنفَال: 17]

Khaled Ibrahim Betala
“Inu simudawaphe (ndi mphamvu zanu) koma Allah ndi Yemwe anawapha; siudawagende pamene udagenda koma Allah ndi amene anawagenda (pofikitsa mchenga m’maso mwawo, wachita zimenezi) kuti awachitire zabwino Asilamu powapatsa dalitso labwino lochokera kwa Iye. Ndithu Allah Ngwakumva, Ngodziwa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek