×

Monga anthu a Farao ndi iwo amene adalipo kale, iwo adakana zizindikiro 8:52 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:52) ayat 52 in Chichewa

8:52 Surah Al-Anfal ayat 52 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 52 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿كَدَأۡبِ ءَالِ فِرۡعَوۡنَ وَٱلَّذِينَ مِن قَبۡلِهِمۡۚ كَفَرُواْ بِـَٔايَٰتِ ٱللَّهِ فَأَخَذَهُمُ ٱللَّهُ بِذُنُوبِهِمۡۚ إِنَّ ٱللَّهَ قَوِيّٞ شَدِيدُ ٱلۡعِقَابِ ﴾
[الأنفَال: 52]

Monga anthu a Farao ndi iwo amene adalipo kale, iwo adakana zizindikiro za Mulungu, ndipo Mulungu adawalanga chifukwa cha kulakwa kwawo. Ndithudi Mulungu ndi wamphamvu ndipo amakhwimitsa chilango

❮ Previous Next ❯

ترجمة: كدأب آل فرعون والذين من قبلهم كفروا بآيات الله فأخذهم الله بذنوبهم, باللغة نيانجا

﴿كدأب آل فرعون والذين من قبلهم كفروا بآيات الله فأخذهم الله بذنوبهم﴾ [الأنفَال: 52]

Khaled Ibrahim Betala
“(Khalidwe lawo awa lili ) ngati khalidwe la anthu a Farawo ndi omwe adalipo patsogolo pawo. Anazikana zizindikiro za Allah, choncho Allah anawalanga chifukwa cha machimo awo. Ndithudi Allah Ngwamphamvu, Wolanga moopsa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek