×

Ichi ndi chifukwa chakuti Mulungu sasintha madalitso amene amapereka kwa anthu mpaka 8:53 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:53) ayat 53 in Chichewa

8:53 Surah Al-Anfal ayat 53 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 53 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿ذَٰلِكَ بِأَنَّ ٱللَّهَ لَمۡ يَكُ مُغَيِّرٗا نِّعۡمَةً أَنۡعَمَهَا عَلَىٰ قَوۡمٍ حَتَّىٰ يُغَيِّرُواْ مَا بِأَنفُسِهِمۡ وَأَنَّ ٱللَّهَ سَمِيعٌ عَلِيمٞ ﴾
[الأنفَال: 53]

Ichi ndi chifukwa chakuti Mulungu sasintha madalitso amene amapereka kwa anthu mpaka pamene iwo asintha makhalidwe awo, ndipo ndithudi, Mulungu ndi wakumva ndi wodziwa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ذلك بأن الله لم يك مغيرا نعمة أنعمها على قوم حتى يغيروا, باللغة نيانجا

﴿ذلك بأن الله لم يك مغيرا نعمة أنعمها على قوم حتى يغيروا﴾ [الأنفَال: 53]

Khaled Ibrahim Betala
“Izo, (posawadzera miliri yotere) nchifukwa chakuti Allah sasintha chisomo (Chake) chimene wachipereka kwa anthu mpaka anthuwo asinthe okha zomwe zili m’mitima mwawo, (posiya kuthokoza Allah nayamba kuyenda m’njira zolakwira Allah). Ndithu Allah Ngwakumva Ngodziwa chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek