×

Ndipo Mulungu sadzasocheretsa anthu amene wawatsogolera pokhapokha Iye wawafotokozera zonse zimene ayenera 9:115 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:115) ayat 115 in Chichewa

9:115 Surah At-Taubah ayat 115 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 115 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿وَمَا كَانَ ٱللَّهُ لِيُضِلَّ قَوۡمَۢا بَعۡدَ إِذۡ هَدَىٰهُمۡ حَتَّىٰ يُبَيِّنَ لَهُم مَّا يَتَّقُونَۚ إِنَّ ٱللَّهَ بِكُلِّ شَيۡءٍ عَلِيمٌ ﴾
[التوبَة: 115]

Ndipo Mulungu sadzasocheretsa anthu amene wawatsogolera pokhapokha Iye wawafotokozera zonse zimene ayenera kuzipewa, Ndithudi Mulungu amadziwa chinthu china chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وما كان الله ليضل قوما بعد إذ هداهم حتى يبين لهم ما, باللغة نيانجا

﴿وما كان الله ليضل قوما بعد إذ هداهم حتى يبين لهم ما﴾ [التوبَة: 115]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah sangasokeretse anthu (ndi kupititsa chilango pa iwo) pambuyo powaongolera ku Chisilamu; koma pokhapokha atawonetsa poyera kwa iwo zimene zingafunike kuzipewa. Ndithu Allah Ngodziwa chilichonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek