×

Nthawi zonse pamene mutu uvumbulutsidwa, iwo amayang’anitsitsana ndi kufunsa kuti: “Kodi akukuonani 9:127 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:127) ayat 127 in Chichewa

9:127 Surah At-Taubah ayat 127 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 127 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿وَإِذَا مَآ أُنزِلَتۡ سُورَةٞ نَّظَرَ بَعۡضُهُمۡ إِلَىٰ بَعۡضٍ هَلۡ يَرَىٰكُم مِّنۡ أَحَدٖ ثُمَّ ٱنصَرَفُواْۚ صَرَفَ ٱللَّهُ قُلُوبَهُم بِأَنَّهُمۡ قَوۡمٞ لَّا يَفۡقَهُونَ ﴾
[التوبَة: 127]

Nthawi zonse pamene mutu uvumbulutsidwa, iwo amayang’anitsitsana ndi kufunsa kuti: “Kodi akukuonani wina aliyense?” Akatero iwo amabwerera m’mbuyo. Mulungu watembenuza mitima yawo, chifukwa iwo ndi anthu osazindikira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا ما أنـزلت سورة نظر بعضهم إلى بعض هل يراكم من أحد, باللغة نيانجا

﴿وإذا ما أنـزلت سورة نظر بعضهم إلى بعض هل يراكم من أحد﴾ [التوبَة: 127]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek