×

Pakati pa Maarabu ena a m’chipululu pali amene amakhulupirira mwa Mulungu ndi 9:99 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:99) ayat 99 in Chichewa

9:99 Surah At-Taubah ayat 99 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 99 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿وَمِنَ ٱلۡأَعۡرَابِ مَن يُؤۡمِنُ بِٱللَّهِ وَٱلۡيَوۡمِ ٱلۡأٓخِرِ وَيَتَّخِذُ مَا يُنفِقُ قُرُبَٰتٍ عِندَ ٱللَّهِ وَصَلَوَٰتِ ٱلرَّسُولِۚ أَلَآ إِنَّهَا قُرۡبَةٞ لَّهُمۡۚ سَيُدۡخِلُهُمُ ٱللَّهُ فِي رَحۡمَتِهِۦٓۚ إِنَّ ٱللَّهَ غَفُورٞ رَّحِيمٞ ﴾
[التوبَة: 99]

Pakati pa Maarabu ena a m’chipululu pali amene amakhulupirira mwa Mulungu ndi tsiku lomaliza, ndipo amaona zopereka zawo m’njira ya Mulungu ngati zinthu zowabweretsa kufupi ndi Mulungu ndi mapemphero a Mtumwi. Ndithudi zimenezo zidzawabweretsa kufupi. Ndipo Mulungu adzawalowetsa iwo ku chisomo chake. Ndithudi Mulungu ndi wokhululukira ndi wachisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ومن الأعراب من يؤمن بالله واليوم الآخر ويتخذ ما ينفق قربات عند, باللغة نيانجا

﴿ومن الأعراب من يؤمن بالله واليوم الآخر ويتخذ ما ينفق قربات عند﴾ [التوبَة: 99]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo alipo ena mwa Arabu a kuchimizi omwe akukhulupirira Allah ndi tsiku lachimaliziro ndipo zomwe akupereka (pa njira ya Allah) amazichita monga chodziyandikitsira nacho kwa Allah, ndi (chowachititsa kuti apeze) mapemphero a Mtumiki. Tamverani! Ndithu zimenezo ndizinthu zowayandikitsa kwa Allah. Allah adzawalowetsa ku Mtendere Wake. Ndithu Allah Ngokhululuka kwambiri, Ngwachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek