×

Ndipo iwo amene adalowa Chisilamu poyamba, kuchokera ku gulu limene lidachoka ku 9:100 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:100) ayat 100 in Chichewa

9:100 Surah At-Taubah ayat 100 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 100 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿وَٱلسَّٰبِقُونَ ٱلۡأَوَّلُونَ مِنَ ٱلۡمُهَٰجِرِينَ وَٱلۡأَنصَارِ وَٱلَّذِينَ ٱتَّبَعُوهُم بِإِحۡسَٰنٖ رَّضِيَ ٱللَّهُ عَنۡهُمۡ وَرَضُواْ عَنۡهُ وَأَعَدَّ لَهُمۡ جَنَّٰتٖ تَجۡرِي تَحۡتَهَا ٱلۡأَنۡهَٰرُ خَٰلِدِينَ فِيهَآ أَبَدٗاۚ ذَٰلِكَ ٱلۡفَوۡزُ ٱلۡعَظِيمُ ﴾
[التوبَة: 100]

Ndipo iwo amene adalowa Chisilamu poyamba, kuchokera ku gulu limene lidachoka ku Makka ndi ku Medina, ndi ena amene anawatsatira. Mulungu ndi wosangalala kwambiri ndi iwo monga momwe iwo ali osangalalandi Iye. Iyewawakonzeramindayothiriridwandi madzi a mitsinje yoyenda pansi pake kumene adzakhalako mpaka kalekale. Kumeneku ndiko kupambana kwakukulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والسابقون الأولون من المهاجرين والأنصار والذين اتبعوهم بإحسان رضي الله عنهم ورضوا, باللغة نيانجا

﴿والسابقون الأولون من المهاجرين والأنصار والذين اتبعوهم بإحسان رضي الله عنهم ورضوا﴾ [التوبَة: 100]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene adatsogolera poyamba, a m’gulu la Amuhajirina ndi Answari, ndi omwe adawatsatira iwo mwa ubwino, Allah adzakondwa nawo. Naonso adzakondwera Naye (pa zomwe adzapatsidwa ndi Allah). Ndipo wawakonzera minda yomwe mitsinje ikuyenda pansi (ndi pasogolo) pake, adzakhala m’menemo muyaya. Uko ndikupambana kwakukulu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek