×

Akadakhala kuti Mulungu amabweretsa msanga chilango kwa anthu monga momwe iwo amafunira 10:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:11) ayat 11 in Chichewa

10:11 Surah Yunus ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 11 - يُونس - Page - Juz 11

﴿۞ وَلَوۡ يُعَجِّلُ ٱللَّهُ لِلنَّاسِ ٱلشَّرَّ ٱسۡتِعۡجَالَهُم بِٱلۡخَيۡرِ لَقُضِيَ إِلَيۡهِمۡ أَجَلُهُمۡۖ فَنَذَرُ ٱلَّذِينَ لَا يَرۡجُونَ لِقَآءَنَا فِي طُغۡيَٰنِهِمۡ يَعۡمَهُونَ ﴾
[يُونس: 11]

Akadakhala kuti Mulungu amabweretsa msanga chilango kwa anthu monga momwe iwo amafunira zabwino kuti zidze mwansanga, nthawi yawo yofera ikadakwaniritsidwa. Kwa iwo amene saopa kukumana ndi Ife tidzawasiya mukusochera kwawo, akusowa chochita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو يعجل الله للناس الشر استعجالهم بالخير لقضي إليهم أجلهم فنذر الذين, باللغة نيانجا

﴿ولو يعجل الله للناس الشر استعجالهم بالخير لقضي إليهم أجلهم فنذر الذين﴾ [يُونس: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Allah akadakhala kuti akuwapatsa anthu zoipa mwachangu (zomwe iwo akuzifulumizitsa) monga mmene amawapatsira mwachangu zabwino (akamupemphamo, ndiye kuti) ikadalamulidwa nthawi yawo (yowaonongera koma Allah amawamvera chisoni), koma amene saopa kukumana Nafe tikuwasiya akuyumbayumba m’zoipa zawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek