×

Pamene mavuto amadza pa munthu, iye amapemphera kwa Ifemogonachanthiti, mokhalapansikapenamoimirira. Koma tikangomuchotsera 10:12 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:12) ayat 12 in Chichewa

10:12 Surah Yunus ayat 12 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 12 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَإِذَا مَسَّ ٱلۡإِنسَٰنَ ٱلضُّرُّ دَعَانَا لِجَنۢبِهِۦٓ أَوۡ قَاعِدًا أَوۡ قَآئِمٗا فَلَمَّا كَشَفۡنَا عَنۡهُ ضُرَّهُۥ مَرَّ كَأَن لَّمۡ يَدۡعُنَآ إِلَىٰ ضُرّٖ مَّسَّهُۥۚ كَذَٰلِكَ زُيِّنَ لِلۡمُسۡرِفِينَ مَا كَانُواْ يَعۡمَلُونَ ﴾
[يُونس: 12]

Pamene mavuto amadza pa munthu, iye amapemphera kwa Ifemogonachanthiti, mokhalapansikapenamoimirira. Koma tikangomuchotsera mavuto ake, iye amatsatila njira zake kukhala ngati sadatipemphe kuti timuchotsere mavuto omwe adamupeza. Kotero zidakongoletsedwa kwa anthu oononga zimene anali kuchita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذا مس الإنسان الضر دعانا لجنبه أو قاعدا أو قائما فلما كشفنا, باللغة نيانجا

﴿وإذا مس الإنسان الضر دعانا لجنبه أو قاعدا أو قائما فلما كشفنا﴾ [يُونس: 12]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo vuto likamkhuza munthu amatipempha (m’kakhalidwe kake konse), chogona, chokhala kapena choimilira. Koma tikamchotsera vuto lomwe lidampeza, amayenda ngati sanatipempheko pa vuto Iomwe Iidamkhudza. Momwemo ndimo zakometseredwa kwa opyola malire zomwe ankachita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek