×

Anthu osakhulupirira amanena kuti: “Kodi chifukwa ninji chizindikiro sichinaperekedwe kwa iye kuchokera 10:20 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Yunus ⮕ (10:20) ayat 20 in Chichewa

10:20 Surah Yunus ayat 20 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Yunus ayat 20 - يُونس - Page - Juz 11

﴿وَيَقُولُونَ لَوۡلَآ أُنزِلَ عَلَيۡهِ ءَايَةٞ مِّن رَّبِّهِۦۖ فَقُلۡ إِنَّمَا ٱلۡغَيۡبُ لِلَّهِ فَٱنتَظِرُوٓاْ إِنِّي مَعَكُم مِّنَ ٱلۡمُنتَظِرِينَ ﴾
[يُونس: 20]

Anthu osakhulupirira amanena kuti: “Kodi chifukwa ninji chizindikiro sichinaperekedwe kwa iye kuchokera kwa Ambuye wake?” Nena, “Mulungu yekha ndiye amene amadziwa chilichonse chobisika. Dikirani, nanenso ndili mmodzi mwa odikira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويقولون لولا أنـزل عليه آية من ربه فقل إنما الغيب لله فانتظروا, باللغة نيانجا

﴿ويقولون لولا أنـزل عليه آية من ربه فقل إنما الغيب لله فانتظروا﴾ [يُونس: 20]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo akunena: “Kukadakhala kuti chinatsitsidwa kwa iye chizindikiro (chotsimikizira uneneri wake) chochokera kwa Mbuye wake (chomwe takhala tikuchipempha nthawi ndi nthawi).” Nena (kwa iwo): “Ndithu kudziwa zobisika nkwa Allah Yekha. Choncho dikirani (chiweruzo cha Allah) inenso pamodzi nanu ndine mmodzi wa odikira.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek